Nyimbo Ikatha Lyrics
- Genre:Gospel
- Year of Release:2021
Lyrics
Nyimbo Ikatha - Kelvin Sings
...
Kunja kwacha (mavuto ndi omwewa koma tsiku langosintha)
Mdima wagwa(nyimbo ndi yomweyi koma oyimba wango sintha)
Mtima wanga umasweka kale pena ndi yesa ngati ndilibe m'bale
Kusowa oti angandithangate
Tsogolo looneka lopuwala komabe ndiimaba(mwina mavuto nkuzilala)
Misonzi I Kamanga nyumba pamasaya
Confort me zitolilo ndi gitala
Ndikakhala chete makutu mwanga mumaveka nyimbo for some time mtimawu supweteka chowawa chimagwera mkati
Mayeselo a moyo wanga (nyimbo ndi likasa)
Nkhawa ine nkhawa ine (nyimbo ikatha)
Nyimbo ikatha (ndiyimbebe)
Nyimbo ikatha (ndimbebe)
Coz as it plays I'm alright I'm alright I'm alright
Maloto anga ndimalota ndili ntchana
Anthu ambili dzina langa akuliyitana
Mayi anga kusekelela akandiyang'ana
But later on reality strike and am back with MI fellas chilling on the block and the sun rise and it set we are watching we pray fi di blessings we grind till we hafitt but
Whom jahjah blessed though no man can curse now blage yala strum ikaso drum tiyimbe nkhawa tipachike
Poti tikakhala chete makutu mwanga mumaveka nyimbo
For some time mtimawu supweteka chowawa chimagwera mkati
Mayesero a moyo wanga (nyimbo ndi likasa)
Nkhawa ine nkhawa ine (nyimbo ikatha)
Nyimbo ikatha (ndiimbebe)
Nyimbo ikatha(ndiyimbebe)
Coz as it plays am alright am alright am alright
Mayesero a moyo wanga nyimbo ndi likasa
Nkhawa ine nkhawa ine (nyimbo ikatha)
Nyimbo ikatha(ndiyimbebe)
Nyimbo ikatha(ndiyimbebe)
Cos as it plays I'm alright am alright am alright