Mamuna Amene Ndili Lyrics
- Genre:Soul
- Year of Release:2020
Lyrics
Mamuna Amene Ndili - Kelvin Sings
...
unandipeza ndili lova
ndilibe kalikonse
m'matumba mwanga mobooka
nyumba yopanda khonde
ndekuti dzuwa likawomba
nkati khuma kumaonda
iweyo utandiona
simvetsa chomwe unakondaaa
utabwera unandilimbikitsa unati ndisabwerere m'mbuyo
chomwe chinali chako nanenso ndi changa kuti ndisamasowe tulo
you must be a Saint or something
how could you give it all and ask for nothing in return now yah
ndikusowa chonena ine
malangizo ako
andifikitsa pena ine
poti ndine wako
Bwera umunyadire mamuna Amene Ndili kamba ka iwe
bwera umunyadire mamuna Amene Ndili kamba ka iwe
for i was never enough
i had room for you my bae
ndidzizwa ndi chisankho chako
chokhala nane ngakhale munyumba mwanga mpando munalibe
pomwe sizinkandiyendera
unagwada ndikupemphera
pamene mwayi unasendera
unandiuza ndimukumbuke Namalenga
ndikamabwera ku ulenje
m'malo mwa nyama ndi denje
nkumandilandirabe ndi chimwemwe ine pakamwa kakasi
you know pena nkati ndidye frus
rest of my days i am under the weather
but i believe GOD gave you to me to help me keep it together
you must be a Saint or something
how could you give it all and ask for nothing in return now yah
ndikusowa chonena ine
malangizo ako
andifikitsa pena ine
poti ndine wako
bwera umunyadire mamuna Amene Ndili kamba ka iwe
bwera umunyadire mamuna Amene Ndili kamba ka iwe
bwera umunyadire mamuna Amene Ndili kamba ka iwe
bwera umunyadire mamuna Amene Ndili kamba ka iwe
ndikusowa chonena ine
malangizo ako
andifikitsa pena ine
poti ndine wako
bwera umunyadire mamuna amene ndili kamba ka iwe
bwera umunyadire mamuna amene ndili kamba ka iwe