Kondela Lyrics
- Genre:Gospel
- Year of Release:2023
Lyrics
Kondela - D-Spencer 97
...
KONDELA lyrics
9seven
Yeah (aaa aah mumandikondela)
D Brotherz, D-Spencer (aaa aah mumandikondela)
Siine wochenjera kupezeka ndili moyo
Nane sindimvetsa nthawi yomwe ndilimoyo
Madalitso mbwee, kundipatsa nditangodekha
Kupempha chimodzi ndikundipatsa double decker
Munandipatsa vep, apa ndikupeza cash
Ndikudyanso bhooo, hmm hmm Squash
Nzeru zanga zikangotha inu mmayamba pompo
Pakhudza dzanja lanu moyo ukumayenda bhobho
Zomwe ine Mbuye andipangira
Akuona ngati ndikuphangira
Nkamaona zonse mwandipatsira
Inu Mbuye wanga m’makwanira
Mumandikondela
Aaa aah mumandikondela
Mumandikondela
Inu Mbuye wanga mumandikondela
Kondela, kondela
Aaa aah mumandikondela
Kondela, kondela
Aaa aah mumandikondela
Mwawala m’moyo wanga ndithu kuposa magetsi
Mpake ndikukondwa uku ndikudropa ma verse
Mmathana ndi zina zoti ineyo nsakudziwa
Kuthana ndi nkhondo zoti ineyo sindingathe
Mmakonza njira ngati pa nyanja ndi Mose
Mpake ndikuimba olo ndikuyuza mose
Chifukwa cha inu nyengo zanga zinasinthano
Ndipo ndawonadi mau anuwa si nthano
Zomwe ine Mbuye andipangira
Akuona ngati ndikuphangira
Nkamaona zonse mwandipatsira
Inu Mbuye wanga m’makwanira
Mumandikondela
Aaa aah mumandikondela
Mumandikondela
Inu Mbuye wanga mumandikondela
Kondela, kondela
Aaa aah mumandikondela
Kondela, kondela
Aaa aah mumandikondela
Ena akufunsa, “akuimba uku ndani?”
Ena akudabwa, akuimba hook ndani
Ena kundithoka Spencer Ambuye akukondani
Moti sindidanda kuti mawa ndidya chani
Ati ndikuzipopa, ine shaaa! Eya poti,
Ndathera pa inu ngati ndege pa airport
Mwandipatsa dola, ana, mphatso
Akazi onsewa munandipatsa wanga, that’s all