Ndakulila ft. Charisma Madness Lyrics
- Genre:Hip Hop & Rap
- Year of Release:2023
Lyrics
Ndinkakuphwekesa poti unkakhala pambali
Ndinkangokuyesa mwina sungandithawe
Ndinkakuchedwesa kumakutaisa nthawi
Ndinkangoyesa mwina sungandithawe
Koma pano ine ndakulila
Ine ndakulila
Ineyo nde ndakulila
mmmh ndakulila
Koma pano ine ndakulila
Ine ndakulila
Ubwelele ine ndakulila
Aa aaaa aa aaa aaa
Love of my life
One of the kind
Nnali Steve wonder ndinali blind
Olo ndekha simpanga understand
Nali ndi Mvuto, nali ndi carnal mind
Chibwezi chongokhalila ma fights
Zachikondi panalibepo ayi
Pano ndataya chi dynamite
I'm just tryna make things right yeah
Kodi ngakuwine bwanji
Won't play games like jumanji
Babe tandipatse mtaji
I like the way you call me daddy
Linda bwelela, tizasungane
Ndizizakuvela, kuti tisakangane
You know the road when you missing home
You know it's cold when the sun is gone cold!
You know a lover when you let her go! You know!
Oooh oooooh oh!
Ndinkakuphwekesa poti unkakhala pambali
Ndinkangokuyesa mwina sungandithawe
Ndinkakuchedwesa kumakutaisa nthawi
Ndinkangoyesa mwina sungandithawe
Koma pano ine ndakulila
Ine ndakulila
Ineyo nde ndakulila
mmmh ndakulila
Koma pano ine ndakulila
Ine ndakulila
Ubwelele ine ndakulila
Aa aaaa aa aaa aaa
Zibwana nnapanga nnapanga zosiyana
Pano kukuitana mamie mumandikana
I need you back babe
I am missing you daily
Ndasowa zathu zose tinkapanga tinangosiyana malele
I'm on my knees, I'm begging you
I'm saying please, pano ine sindingakunamize
singakuike pa easy
Ayi ayi pano babe ine ndikupatsa iwe zose
Ndikukonde ndi mtima wanga ndi thupi langa lose
You know the road when you missing home
You know it's cold when the sun is gone
You know a lover when you let her go!
Oooh oooooh oh!
Ndinkakuphwekesa poti unkakhala pambali
Ndinkangokuyesa mwina sungandithawe
Ndinkakuchedwesa kumakutaisa nthawi
Ndinkangoyesa mwina sungandithawe
Koma pano ine ndakulila
Ine ndakulila
Ineyo nde ndakulila
mmmh ndakulila
Koma pano ine ndakulila
Ine ndakulila
Ubwelele ine ndakulila
Aa aaaa aa aaa aaa