Anakonza ft. Kelvin Sings Lyrics
- Genre:Gospel
- Year of Release:2022
Lyrics
Anakonza ft. Kelvin Sings - Mastol
...
kuwala kwako ngakhale dzuwa limaimika manjaaa
naponda potani kuti weyo ukhale wangaa
analenga nyenyezi ndi dzuwa
ndiye amend nalenga iweee....
mfuna zizakathele paguwa
mntima wanga watenga ndiwee...eeeh ... eeeh oooaahh.
mtima wanga unasweka zinatsala ndi zidutswa.
Nde nkhani zachikondi mmazileka zizidutsa.
sindinkafuna olo kumva nnasanduka gonthi.
my mtima munadzadza ndi milandi ngati khothi.
ena ankaunena mtima wanga ati ndiwo.... vuta kuukonda ...
mwina umafila aunt tiwo ...
anzanga mmawashisha akafunsa ngati ndiwo.... anapangitsa kuti ine nzikhalabe single...
ntakumana ndiwe dziko linayamba kuzuna .
anthu anadziwa nthumwi wapeza katsuna .
thupi losalala ngati sadwala malungo.